Langwan Piksy - Maso Lyrics
VERSE 1NdakhalilidwaNdakankhidwaNdakanidwaNdasalidwaNdapanidwaBut I didnt go downYeah ena ankati sindingazitheMalo ena sinnapiteZinawawa koma look at me nowEyYou know, nthawi zina tima manga ndende tokhaZabwino zochulukitsa tokha tima blockerTimafuna zophweka zikavuta tima dropperKudikira ena ayambe ife tingokopaAnthu ochuluka they wanna see me beggingKuyamba ngati othandiza they wanna leave me hangingPankhope ngati a chifundo but I know they fakingPankhope a chikondi kumbaliko nde ndisekeniPeople take your kindness for a weaknessKusiya zawo uko they mind your businessYou know, sometimes ndi bwino kumasunga chinsinsiKukhala wekha bola mu mtima wako muli peace(amen)CHORUSSo many things I can thank god forMadalitso ndaona ndi masoAnali nane pompoPomwe panali khoma anayikapo khomoYeahSo many things I can thank God forMadalitso ndawaona ndi masoZomwe ankati sizingandichitikireNdaziona ndi masoVERSE 2Musanandide mufunse komwe ndachokaMukanakhala ine ena a inu mukanafokaI lost hopeIt got too hard to copeEverything felt so wrongMan its been
.hard for meMaloto far from realLero mphamvu ndzipeza ain no stopping meNdingati ku maloto nkamaona successOnse munayima nane nyengo iyi God blessWhoever thought ndidzafika this far?Ndinali mnyamata pano ndi MisterAnthu ochuluka callin me starNsanje ayi mudzinditcha victorLero zinthu zimasintha when I step inMphepo ingadze molimba im not shakenNdimangosekaZikuphwekaMulungu wadalitsa zonse zongothekaCHORUSSo many things I can thank god forMadalitso ndaona ndi masoAnali nane pompoPomwe panali khoma anayikapo khomoYeahSo many things I can thank God forMadalitso ndawaona ndi masoZomwe ankati sizingandichitikireNdaziona ndi masoVERSE 3Anthu amene andikondane zeni zeni(ndawaona ndi maso)Adani anga onse ali pa ntetete(ndawaona ndi maso)Chisomo chanu position kuchita maintain(ndachiona ndi maso)Chikondi ndachiona ndi maso
maso
masoCHORUSSo many things I can thank god forMadalitso ndaona ndi masoAnali nane pompoPomwe panali khoma anayikapo khomoYeahSo many things I can thank God forMadalitso ndawaona ndi masoZomwe ankati sizingandichitikireNdaziona ndi maso